Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 22:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Utero msonkhano wonse wa Yehova, Colakwa ici nciani mwalakwira naco Mulungu wa Israyeli, ndi kumtembenukira Yehova lero line kusamtsatanso, popeza munadzimangira guwa la nsembe kupikisana ndi Yehova lero lino?

Werengani mutu wathunthu Yoswa 22

Onani Yoswa 22:16 nkhani