Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 22:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ana a Israyeli anamva anthu akuti, Taonani ana a Rubeni, ndi ana a Gadi, ndi pfuko la Manase logawika pakati anamanga guwa la nsembe pandunji pa dziko la Kanani, ku mbali ya ku Yordano, ku mbali ya ana a Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 22

Onani Yoswa 22:11 nkhani