Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 21:29-32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

29. Yarimutu ndi mabusa ace, Eniganimu ndi mabusa ace; midzi inai.

30. Ndipo motapira pa pfuko La Aseri, Misali ndi mabusa ace, Abidoni ndi mabusa ace;

31. Helikati ndi mabusa ace, ndi Rehobo ndi mabusa ace; midzi inai.

32. Ndipo motapira pa pfuko la Nafitali, Kedesi m'Galileya ndi mabusa ace, ndiwo mudzi wopulumukirako wakupha mnzaceyo, ndi Hamotidori ndi mabusa ace, ndi Karitani ndi mabusa ace, midzi itatu.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 21