Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 20:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Iyi ndi midzi yoikidwira ana onse a Israyeli, ndi mlendo wakukhala pakati pao, kuti athawireko ali yense wakupha munthu, ndi kuti asafe ndi dzanja la wolipsa mwazi, asanaime pamaso pa msonkhano.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 20

Onani Yoswa 20:9 nkhani