Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 19:23-26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

23. Ici ndi colowa ca pfuko la ana a Isakara, monga mwa mabanja ao, midzi ndi miraga yao.

24. Ndipo maece acisanu analiturukira pfuko la ana a Aseri monga mwa mabanja ao.

25. Ndi malire ao ndiwo Helikati, ndi Hali, ndi Beteni ndi Akisafu;

26. ndi Alameleki, ndi Amadi, ndi Misali; nafikira ku Karimeli kumadzulo ndi ku Sihorilibinati;

Werengani mutu wathunthu Yoswa 19