23. Ici ndi colowa ca pfuko la ana a Isakara, monga mwa mabanja ao, midzi ndi miraga yao.
24. Ndipo maece acisanu analiturukira pfuko la ana a Aseri monga mwa mabanja ao.
25. Ndi malire ao ndiwo Helikati, ndi Hali, ndi Beteni ndi Akisafu;
26. ndi Alameleki, ndi Amadi, ndi Misali; nafikira ku Karimeli kumadzulo ndi ku Sihorilibinati;