Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 17:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anayandikira pamaso pa Eleazare wansembe, ndi pamaso pa Yoswa mwana wa Nuni, ndi pamaso pa akalonga, ndi kuti, Yehova analamulira Mose atipatse colowa pakati pa abale athu; cifukwa cace anawapatsa monga mwa lamulo La Yehova, colowa pakati pa abale a atate wao.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 17

Onani Yoswa 17:4 nkhani