Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 17:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Gawo la pfuko la Manase ndi ili: pakuti anali woyamba wa Yosefe. Makiri mwana woyamba wa Manase, atate wa Gileadi, popeza ndiye munthu wa nkhondo, anakhala nayo Gileadi ndi Basana.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 17

Onani Yoswa 17:1 nkhani