Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 15:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi malire a kum'mawa ndiwo Nyanja ya Mcere, mpaka mathiriro ace a Yordano. Ndi malire a kumpoto anayambira nyondo ya nyanja ku mathiriro a Yordano;

Werengani mutu wathunthu Yoswa 15

Onani Yoswa 15:5 nkhani