Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 15:47-55 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

47. Asidodo, midzi yace ndi miraga yace; Gaza, midzi yace ndi miraga yace; mpaka mtsinje wa Aigupto, ndi nyanja yaikuru ndi malire ace.

48. Ndi kumapiri Samiri, ndi Yatiri, om Soko;

49. ndi Dana, ndi Kiriyatisana, ndiwo Dibiri;

50. ndi Anabi, ndi Esitemo, ndi Animu;

51. ndi Goseni, ndi Holoni, ndi Gilo; midzi khumi ndi umodzi pamodzi ndi miraga yao.

52. Arabu, ndi Duma, ndi Esana;

53. ndi Yanimu, ndi Beti-tapua, ndi Apeka;

54. ndi Humita, ndi Kiriyatiariba, ndiwo Hebroni, ndi Ziori; midzi isanu ndi inai pamodzi ndi miraga yao.

55. Maoni, Karimeli, ndi Zifu, ndi Yuta;

Werengani mutu wathunthu Yoswa 15