Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 15:35-54 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

35. Yarimutu, ndi Adulamu, Soko, ndi Azeka;

36. ndi Saaraimu, ndi Aditaimu, ndi Gedera, ndi Gederotaimu; midzi khumi ndi inai pamodzi ndi miraga yao.

37. Zenani, ndi Hadasa, ndi Migidala-gadi;

38. ndi Dilani, ndi Mizipe, ndi Yokiteeli;

39. Lakisi ndi Bozikatu ndi Egiloni;

40. ndi Kaboni, ndi Lamasi, ndi, Kitilisi;

41. ndi Gaderotu, Beti-dagoni, ndi Naama, ndi Makeda; midzi khumi ndi isanu ndi umodzi pamodzi ndi miraga yao.

42. Libina ndi Eteri ndi Asana;

43. ndi Ifita ndi Asina ndi Nezibi;

44. ndi Kehila ndi Akisibu, ndi Maresa; midzi isanu ndi inai pamodzi ndi miraga yao.

45. Ekroni pamodzi ndi midzi yace ndi miraga yao;

46. kuyambira ku Ekroni mpaka kunyanja, yonse ya ku mbali ya Asidodo, pamodzi ndi miraga yao.

47. Asidodo, midzi yace ndi miraga yace; Gaza, midzi yace ndi miraga yace; mpaka mtsinje wa Aigupto, ndi nyanja yaikuru ndi malire ace.

48. Ndi kumapiri Samiri, ndi Yatiri, om Soko;

49. ndi Dana, ndi Kiriyatisana, ndiwo Dibiri;

50. ndi Anabi, ndi Esitemo, ndi Animu;

51. ndi Goseni, ndi Holoni, ndi Gilo; midzi khumi ndi umodzi pamodzi ndi miraga yao.

52. Arabu, ndi Duma, ndi Esana;

53. ndi Yanimu, ndi Beti-tapua, ndi Apeka;

54. ndi Humita, ndi Kiriyatiariba, ndiwo Hebroni, ndi Ziori; midzi isanu ndi inai pamodzi ndi miraga yao.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 15