Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 15:31-45 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

31. ndi Zikilaga, ndi Madimana ndi Sanasana;

32. ndi Lebaoti, ndi Siliimu, ndi Aini ndi Rimoni; midzi yonse ndiyo makumi awiri kudza isanu ndi inai; pamodzi ndi miraga yao.

33. Ku cigwa, Esitaoli, ndi Zora ndi Asina;

34. ndi Zoona, ndi Eniganimu, Tapua, ndi Enamu;

35. Yarimutu, ndi Adulamu, Soko, ndi Azeka;

36. ndi Saaraimu, ndi Aditaimu, ndi Gedera, ndi Gederotaimu; midzi khumi ndi inai pamodzi ndi miraga yao.

37. Zenani, ndi Hadasa, ndi Migidala-gadi;

38. ndi Dilani, ndi Mizipe, ndi Yokiteeli;

39. Lakisi ndi Bozikatu ndi Egiloni;

40. ndi Kaboni, ndi Lamasi, ndi, Kitilisi;

41. ndi Gaderotu, Beti-dagoni, ndi Naama, ndi Makeda; midzi khumi ndi isanu ndi umodzi pamodzi ndi miraga yao.

42. Libina ndi Eteri ndi Asana;

43. ndi Ifita ndi Asina ndi Nezibi;

44. ndi Kehila ndi Akisibu, ndi Maresa; midzi isanu ndi inai pamodzi ndi miraga yao.

45. Ekroni pamodzi ndi midzi yace ndi miraga yao;

Werengani mutu wathunthu Yoswa 15