Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 13:30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo malire ao anayambira ku Mahanaimu, Basana lonse, ufumu wonse wa Ogi mfumu ya ku Basana, ndi midzi yonse ya Yairi, yokhala m'Basana, midzi makumi asanu ndi limodzi;

Werengani mutu wathunthu Yoswa 13

Onani Yoswa 13:30 nkhani