Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 12:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo awa ndi mafumu a dzikolo amene Yoswa ndi ana a Israyeli anawakantha tsidya lija la Yordano kumadzulo, kuyambira Baala-gadi m'cigwa ca Lebano mpaka phiri la Halaki lokwera kumka ku Seiri; ndipo Yoswa analipereka kwa mapfuko a Israyeli, likhale lao lao, monga mwa magawo ao;

Werengani mutu wathunthu Yoswa 12

Onani Yoswa 12:7 nkhani