Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 1:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

mpaka Yehova atapatsa abale anu mpumulo, monga umo anakuninkhirani inu, naonso alandira dzikolo awaninkha Yehova Mulungu wanu; pamenepo mubwerere ku dziko lanu lanu, ndi kukhala nalo, limene Mose mtumiki wa Yehova anakupatsani tsidya lino la Yordano la kum'mawa,

Werengani mutu wathunthu Yoswa 1

Onani Yoswa 1:15 nkhani