14. Inde mungakhale munena, Sindimpenya,Mlanduwo uli pamaso pace, ndipo mumlindira.
15. Ndipo tsopano popeza analibe kumzonda m'kukwiya kwace,Ndi kusamalitsa colakwa,
16. Cifukwa cace Yobu anatsegula pakamwa pace mwacabe,Nacurukitsa mau opanda nzeru.