Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 35:12-15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

12. Apo apfuula, koma Iye sawayankha;Cifukwa ca kudzikuza kwa anthu oipa.

13. Zedi Mulungu samvera zacabe,Ndi Wamphamvuyonse sazisamalira.

14. Inde mungakhale munena, Sindimpenya,Mlanduwo uli pamaso pace, ndipo mumlindira.

15. Ndipo tsopano popeza analibe kumzonda m'kukwiya kwace,Ndi kusamalitsa colakwa,

Werengani mutu wathunthu Yobu 35