1. Ndipo Elihu anabwereza kunena, nati,
2. Kodi muciyesa coyenera,Umo mukuti, Cilungamo canga ciposa ca Mulungu,
3. Pakuti munena, Upindulanji naco?Posacimwa ndinapindula ciani cimene sindikadapindula pocimwa?
4. Ndidzakuyankhani,Ndi anzanu pamodzi ndi inu.