Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 26:13-14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

13. Mwa mzimu wace anyezimiritsa thambo;Dzanja lace linapyoza njoka yothawayo.

14. Taonani, awa ndi malekezero a njira zace;Ndi cimene tikumva za Iye ndi cinong'onezo cacing'ono;Koma kugunda kwa mphamvu yace akuzindikiritsa ndani?

Werengani mutu wathunthu Yobu 26