Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 24:6-11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Atema dzinthu zao m'munda;Natola khunkha m'munda wampesa wa woipa.

7. Agona amarisece usiku wonse opanda cobvala,Alibe copfunda pacisanu.

8. Abvumbwa ndi mvula kumapiri,Nafukata thanthwe posowa pousapo.

9. Akwatula wamasiye kubere,Natenga cikole cobvala ca osauka;

10. Momwemo ayenda amarisece opanda cobvala,Nasenza mtolo wa dzinthu ali ndi njala.

11. M'kati mwa malinga a iwo aja ayenga mafuta;Aponda mphesa moponderamo, namva ludzu.

Werengani mutu wathunthu Yobu 24