Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 23:9-14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. Akacita Iye kulamanzere, sindimpenyerera;Akabisala kulamanja, sindimuona,

10. Koma adziwa njira ndilowayi;Atandiyesa ndidzaturuka ngati golidi.

11. Phazi langa lagwiratu moponda Iye,Ndasunga njira yace, wosapambukamo.

12. Sindinabwerera kusiya malamulo a pa milomo yace;Ndasungitsa mau a pakamwa pace koposa lamulo langa langa.

13. Koma Iye ndiye wa mtima umodzi, adzambweza ndani?Ndi ici cimene moyo wace ucifuna acicita.

14. Pakuti adzacita condiikidwiratu;Ndipo zambiri zotere ziri ndi Iye.

Werengani mutu wathunthu Yobu 23