Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 7:6-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Tiyeni, tikwere, timenyane ndi Yuda, timbvute; tiyeni, tidzigumulire mpata, pamenepo tikhazike mfumu pakati pace, ngakhale mwana wamwamuna wa Tabeeli;

7. atero Ambuye Yehova, Upo wao sudzaimai, sudzacitidwa.

8. Pakuti mutu wa Aramu ndi Damasiko, ndi mutu wa Damasiko ndi Rezini, zisadapite zaka makumi asanu ndi limodzi mphambu zisanu Efraimu adzatyokatyoka, sadzakhalanso mtundu wa anthu;

Werengani mutu wathunthu Yesaya 7