Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 7:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti mutu wa Aramu ndi Damasiko, ndi mutu wa Damasiko ndi Rezini, zisadapite zaka makumi asanu ndi limodzi mphambu zisanu Efraimu adzatyokatyoka, sadzakhalanso mtundu wa anthu;

Werengani mutu wathunthu Yesaya 7

Onani Yesaya 7:8 nkhani