Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 7:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anauza a nyumba ya Davide, kuti Aramu wapangana ndi Efraimu. Ndipo mtima wace unagwedezeka, ndi mtima wa anthu ace, monga mitengo ya m'nkhalango igwedezeka ndi mphepo.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 7

Onani Yesaya 7:2 nkhani