Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 62:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa ca Ziyoni sindidzakhala cete, ndi cifukwa ca Yerusalemu sindidzapuma, kufikira cilungamo cace cidzaturuka monga kuyera, ndi cipulumutso cace monga nyali yoyaka.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 62

Onani Yesaya 62:1 nkhani