Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 61:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti monga dziko liphukitsa mphundu zace, ndi monga munda umeretsa zobzalamo, momwemo Ambuye Yehova adzaphukitsa cilungamo ndi matamando pamaso pa amitundu onse.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 61

Onani Yesaya 61:11 nkhani