Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 61:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndidzakondwa kwambiri mwa Yehova, moyo wanga udzakondwerera mwa Mulungu wanga; pakuti Iye wandibveka ine ndi zobvala za cipulumutso, nandipfunda copfunda ca cilungamo, monga mkwati abvala nduwira, ndi monga mkwatibwi adzikometsa yekha ndi miyala yamtengo.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 61

Onani Yesaya 61:10 nkhani