Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 56:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

naonso ndidzanka nao ku phiri langa lopatulika, ndi kuwasangalatsa m'nyumba yanga yopemphereramo; zopereka zao zopsereza ndi nsembe zao zidzalandiridwa pa guwa la nsembe langa; pakuti nyumba yanga idzachedwa nyumba yopemphereramo anthu onse.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 56

Onani Yesaya 56:7 nkhani