Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 53:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Iye ananyozedwa ndi kukanidwa ndi anthu; munthu wazisoni, ndi wodziwa zowawa; ndipo ananyozedwa monga munthu wombisira anthu nkhope zao; ndipo ife sitinamlemekeza.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 53

Onani Yesaya 53:3 nkhani