Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 52:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti simudzacoka mofulumira, kapena kunka mothawa; pakuti Yehova adzakutsogolerani, ndi Mulungu wa Israyeli adzadikira pambuyo panu.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 52

Onani Yesaya 52:12 nkhani