Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 44:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Wacipala acita zace ndi nsompho, nagwira nchito ndi makala, nafanizira fanolo ndi nyundo, nagwira nchito yace ndi mkono wace wamphamvu; inde, ali ndi njala, ndipo mphamvu zace zilephera; iye samwa madzi, nalefuka.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 44

Onani Yesaya 44:12 nkhani