Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 43:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nyama za m'thengo zidzandilemekeza, ankhandwe ndi nthiwatiwa; cifukwa ndipatsa madzi m'cipululu, ndi mitsinje m'mkhwangwala, ndimwetse anthu anga osankhika;

Werengani mutu wathunthu Yesaya 43

Onani Yesaya 43:20 nkhani