Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 42:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Iwo adzabwezedwa m'mbuyo, adzakhala ndi manyazi ambiri amene akhulupirira mafano osemedwa, nati kwa mafano oyengeka, Inu ndinu milungu yathu.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 42

Onani Yesaya 42:17 nkhani