Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 42:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndidzayendetsa akhungu m'khwalala, limene iwo salidziwa; m'njira zimene iwo sazidziwa ndidzawatsogolera; ndidzawalitsa mdima m'tsogolo mwao, ndi kulungamitsa malo okhota. Zinthu Izi ine ndidzacita, ndipo sindidzawasiya.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 42

Onani Yesaya 42:16 nkhani