Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 38:9-12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. Malemba a Hezekiya mfumu ya Ayuda muja anadwala, atacira nthenda yace.

10. Ine ndinati, Pakati pa masiku anga ndidzalowa m'zipata za kunsi kwa manda; Ndazimidwa zaka zanga zotsala.

11. Ndinati, Sindidzaona Yehova m'dziko la amoyo; sindidzaonanso munthu pamodzi ndi okhala kunja kuno;

12. Pokhala panga pacotsedwa, pandisunthikira monga hema wambusa;Ndapindapinda moyo wanga ngati muomba;Iye adzandidula ine poomberapo;Kuyambira usana kufikira usiku mudzanditsiriza ine.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 38