Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 37:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kapena Yehova Mulungu wako adzamva mau a kazembeyo, amene mfumu ya Asuri mbuyace inamtuma kukatonza Mulungu wamoyo, nadzadzudzula mau amene Yehova Mulungu wako adawamva; cifukwa cace, kweza pemphero lako cifukwa ca otsala osiyidwa.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 37

Onani Yesaya 37:4 nkhani