Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 37:14-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

14. Ndipo Hezekiya analandira kalatayo m'manja mwa mithengayo, namuwerenga; ndipo Hezekiya anakwera kunka ku nyumba ya Yehova, namfunyulula pamaso pa Yehova.

15. Ndipo Hezekiya anapemphera kwa Yehova, nati,

16. Yehova wa makamu, Mulungu wa Israyeli, amene mukhala pa akerubi, Inu ndinu Mulungu, Inu nokha, wa maufumu onse a dziko lapansi, Inu munalenga kumwamba ndi dziko lapansi.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 37