Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 37:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Hezekiya analandira kalatayo m'manja mwa mithengayo, namuwerenga; ndipo Hezekiya anakwera kunka ku nyumba ya Yehova, namfunyulula pamaso pa Yehova.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 37

Onani Yesaya 37:14 nkhani