Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 36:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ukanena kwa ine, Ife tikhulupirira Yehova Mulungu wathu; kodi si ndiye amene Hezekiya wacotsa misanje yace ndi maguwa ace a nsembe, nati kwa Yuda, ndi kwa Yerusalemu, Inu mudzapembedzera patsogolo pa suwa la nsembe ili?

Werengani mutu wathunthu Yesaya 36

Onani Yesaya 36:7 nkhani