Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 36:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anafika Eliakimu, mwana wa Hilikiya, amene anali wapanyumba, ndi Sebina, mlembi, ndi Yoaki, mwana wa Asafu, mkumbutsi, kwa Hezekiya ndi zobvala zao zong'ambika, namuuza iye mau a kazembeyo.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 36

Onani Yesaya 36:22 nkhani