Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 31:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tsoka kwa iwo amene atsikira kunka ku Aigupto kukathandizidwa, natama akavalo; nakhulupirira magareta, pakuti ali ambiri, ndi okwera pa akavalo, pakuti ali a mphamvu zambiri; koma sayang'ana Woyera wa Israyeli, ngakhale kumfuna Yehova!

Werengani mutu wathunthu Yesaya 31

Onani Yesaya 31:1 nkhani