Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 30:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

cifukwa cace kuipa kumeneku kudzakhala kwa inu monga pogumuka pofuna kugwa, monga potukuka m'khoma lalitari, kugumuka kwace kufika modzidzimutsa dzidzidzi.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 30

Onani Yesaya 30:13 nkhani