Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 29:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma khamu la acilendo ako lidzafanana ndi pfumbi losalala, ndi khamu la oopsya lidzakhala monga mungu wocokacoka; inde kudzaoneka modzidzimuka dzidzidzi.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 29

Onani Yesaya 29:5 nkhani