Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 29:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iwe udzagwetsedwa pansi, nudzanena uli pansi, ndi kulankhula kwako kudzakhala pansi koturuka m'pfumbi; ndi mau ako adzakhala ngati a wina amene ali ndi mzimu wobwebweta, kucokera pansi, ndi kulankhula kwako kudzakhala konong'ona kocokera m'pfumbi,

Werengani mutu wathunthu Yesaya 29

Onani Yesaya 29:4 nkhani