Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 28:7-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

7. Koma iwonso adzandima ndi vinyo, nasocera ndi cakumwa caukali, wansembe ndi mneneri adzandima ndi cakumwa caukali, iwo amezedwa ndi vinyo, nasocera ndi cakumwa caukali, adzandima popenya, napunthwa poweruza.

8. Pakuti magome onse adzazidwa ndi masanzi ndi udio, palibe malo okonzeka.

9. Kodi Mulungu adzaphunzitsa yani nzeru? Kodi Iye adzamvetsa yani uthengawo? iwo amene aletsedwa kuyamwa, nacotsedwa pamabere?

Werengani mutu wathunthu Yesaya 28