Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 28:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma iwonso adzandima ndi vinyo, nasocera ndi cakumwa caukali, wansembe ndi mneneri adzandima ndi cakumwa caukali, iwo amezedwa ndi vinyo, nasocera ndi cakumwa caukali, adzandima popenya, napunthwa poweruza.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 28

Onani Yesaya 28:7 nkhani