Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 28:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

cifukwa cace Ambuye Yehova atero, Taonani, ndiika m'Ziyoni mwala wa maziko, mwala woyesedwa mwala wa pangondya, wa mtengo wace wokhazikika ndithu; wokhulupirira sadzafulumira.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 28

Onani Yesaya 28:16 nkhani