Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 25:11-12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. Ndipo iye adzatambasula manja ace pakati pamenepo, monga wosambira atambasula manja ace posambira; koma Iye adzagwetsa pansi kunyada kwace, pamodzi ndi kunyenga kwa manja ace.

12. Ndipo linga la pamsanje la macemba ako Iye waligwetsa, naligonetsa pansi, nalifikitsa padothi, ngakhale papfumbi.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 25