Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 24:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pompo mwezi udzanyazitsidwa, ndi dzuwa lidzakhala ndi manyazi, pakuti Yehova wa makamu adzalamulira caulemerero m'phiri la Ziyoni, ndi m'Yerusalemu, ndi pamaso pa akuru akuru ace.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 24

Onani Yesaya 24:23 nkhani