Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 24:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace padzakhala cotero pakati pa dziko mwa anthu, ngati kugwedeza kwa mtengo waazitona, ngati khunkha la mphesa, pakutha masika ace.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 24

Onani Yesaya 24:13 nkhani