Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 23:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Malonda ace ndi mphotho yace zidzakhala zopatulikira Yehova; sizidzasungidwa kapena kuikidwa; cifukwa malonda ace adzakhala kwa iwo, amene akhala pamaso pa Yehova, kuti adye mokwana, nabvale caulemu.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 23

Onani Yesaya 23:18 nkhani